YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

GENESIS 18 的热门经文

1

GENESIS 18:14

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Kodi chilipo chinthu chomkanika Yehova? Pa nthawi yoikidwa ndidzabwera kwa iwe, pakufika nyengo yake, ndipo Sara adzakhala ndi mwana wamwamuna.

对照

探索 GENESIS 18:14

2

GENESIS 18:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo Sara anaseka m'mtima mwake, nati, Kodi ndidzakhala ndi kukondwa ine nditakalamba, ndiponso mbuyanga ali wokalamba?

对照

探索 GENESIS 18:12

3

GENESIS 18:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakuti Abrahamu adzakhala ndithu wamkulu ndi wamphamvu, ndipo mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsika mwa iye?

对照

探索 GENESIS 18:18

4

GENESIS 18:23-24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Abrahamu anayandikira nati, Kodi mudzaononga olungama pamodzi ndi oipa? Kapena alipo olungama makumi asanu m'kati mwa mudzi; kodi mudzaononga, simudzasiya malowo chifukwa cha olungama makumi asanu ali momwemo?

对照

探索 GENESIS 18:23-24

5

GENESIS 18:26

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Yehova, Ndikapeza m'Sodomu olungama makumi asanu m'kati mwa mudzi, ndidzasiya malo onse chifukwa cha iwo.

对照

探索 GENESIS 18:26

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频