Logotip YouVersion
Sveto pismoBralni načrtiVideoposnetki
Prenesi aplikacijo
Izbirnik jezika
Ikona za iskanje

Priljubljene svetopisemske vrstice iz YOHANE 2

1

YOHANE 2:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chiyambi ichi cha zizindikiro zake Yesu anachita m'Kana wa m'Galileya naonetsera ulemerero wake; ndipo ophunzira ake anakhulupirira Iye.

Primerjaj

Razišči YOHANE 2:11

2

YOHANE 2:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu nanena naye, Mkazi, ndili ndi chiyani ndi inu? Nthawi yanga siinafike.

Primerjaj

Razišči YOHANE 2:4

3

YOHANE 2:7-8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende. Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao.

Primerjaj

Razišči YOHANE 2:7-8

4

YOHANE 2:19

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.

Primerjaj

Razišči YOHANE 2:19

5

YOHANE 2:15-16

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pamene adapanga mkwapulo wazingwe, anatulutsa onse m'Kachisimo, ndi nkhosa ndi ng'ombe; nakhuthula ndalama za osinthanawo, nagubuduza magome; nati kwa iwo akugulitsa nkhunda, Chotsani izi muno; musamayesa nyumba ya Atate wanga nyumba ya malonda.

Primerjaj

Razišči YOHANE 2:15-16

Brezplačni bralni načrti in premišljevanja, povezane z YOHANE 2

Prejšnje poglavje
Naslednje poglavje
YouVersion

Ponujamo ti spodbudo in izziv, da vsak dan iščeš Boga.

Misijonska organizacija

Vizitka

Zaposlitve

Kako postati prostovoljec

Blog

Mediji

Uporabne povezave

Pomoč

Daruj

Prevodi Svetega pisma

Sveto pismo v zvočni obliki

Jeziki, v katerih je na voljo Sveto pismo

Vrstica dneva


Digitalni misijon organizacije

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Pravilnik o zasebnostiPogoji
Program za razkrivanje ranljivosti
FacebookTviterInstagramYouTubePinterest

Domov

Sveto pismo

Bralni načrti

Videoposnetki