Genesis 37:6-7

Genesis 37:6-7 CCL

Iye anawawuza kuti, “Tamvani maloto amene ndinalota: Ife timamanga mitolo ya tirigu ku munda ndipo mwadzidzidzi mtolo wanga unayimirira chilili, pamene mitolo yanu inazungulira mtolo wangawo nʼkumawugwadira.”

Bezpłatne plany czytania i rozważania na temat: Genesis 37:6-7