Logo YouVersion
BibliaPlanyNagrania wideo
Pobierz aplikację
Wybór języka
Ikona wyszukiwania

Popularne wersety biblijne z Gen. 4

1

Gen. 4:7

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Ukadachita zabwino, ndikadakondwera nawe. Koma chifukwa choti wachita zoipa, tchimo lakukhalirira pa khomo ngati chilombo cholusa. Likulakalaka kuti likugwire, koma iweyo uligonjetse tchimolo.”

Porównaj

Przeglądaj Gen. 4:7

2

Gen. 4:26

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Seti adabereka mwana namutcha Enosi. Nthaŵi imeneyo anthu adayamba kutama dzina la Chauta mopemba.

Porównaj

Przeglądaj Gen. 4:26

3

Gen. 4:9

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Tsono Chauta adafunsa Kainiyo kuti, “Kodi mng'ono wako Abele ali kuti?” Iye adayankha kuti, “Sindikudziŵa. Kodi ndi ntchito yanga kusamala mng'ono wangayo?”

Porównaj

Przeglądaj Gen. 4:9

4

Gen. 4:10

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Chauta adamufunsanso kuti, “Kodi wachita chiyani? Magazi a mng'ono wako akulira kwa Ine kuchokera m'nthaka.

Porównaj

Przeglądaj Gen. 4:10

5

Gen. 4:15

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Koma Chauta adamuyankha kuti, “Iyai, aliyense wopha iwe Kaini adzalangidwa, ndipo Ineyo ndidzamulipsira kasanunkaŵiri.” Motero Chauta adaika chizindikiro pa Kaini kuchenjeza aliyense kuti asamuphe Kainiyo.

Porównaj

Przeglądaj Gen. 4:15

Bezpłatne plany czytania i rozważania na temat: Gen. 4

Poprzedni rozdział
Następny rozdział
YouVersion

Zachęcanie i wzywanie cię do codziennego szukania bliskości z Bogiem.

Misja

O YouVersion

Praca

Wolontariat

Blog

Prasa

Przydatne linki

Pomoc

Wesprzyj

Przekłady Biblii

Biblie audio

Języki Biblii

Werset dnia


Cyfrowa misja

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Polityka prywatnościRegulamin
Program ujawniania luk w zabezpieczeniach
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Strona główna

Biblia

Plany

Nagrania wideo