Logo YouVersion
BibliaPlanyNagrania wideo
Pobierz aplikację
Wybór języka
Ikona wyszukiwania

Popularne wersety biblijne z Genesis 41

1

Genesis 41:16

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yosefe anamuyankha Farao kuti, “Sindingathe koma Mulungu apereka yankho limene Farao akufuna.”

Porównaj

Przeglądaj Genesis 41:16

2

Genesis 41:38

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Choncho Farao anafunsa nduna zake nati, “Kodi tingathe kumupeza munthu wina ngati uyu, amene ali ndi mzimu wa Mulungu?”

Porównaj

Przeglądaj Genesis 41:38

3

Genesis 41:39-40

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Farao anati kwa Yosefe, “Pakuti Mulungu wakudziwitsa iwe zonsezi, palibe wina wodziwa zinthu ndi wanzeru ngati iwe. Iwe ukhala nduna yayikulu mu dziko langa ndipo anthu onse adzamvera zimene walamula. Ine ndekha ndiye amene ndidzakuposa mphamvu chifukwa ndimakhala pa mpando waufumu.”

Porównaj

Przeglądaj Genesis 41:39-40

4

Genesis 41:52

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Mwana wachiwiri wa mwamuna anamutcha Efereimu popeza anati, “Mulungu wandipatsa ana mʼdziko la masautso anga.”

Porównaj

Przeglądaj Genesis 41:52

5

Genesis 41:51

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yosefe anamutcha mwana wake woyamba, Manase popeza anati, “Mulungu wandiyiwalitsa zovuta zanga zija ndiponso banja la abambo anga.”

Porównaj

Przeglądaj Genesis 41:51

Bezpłatne plany czytania i rozważania na temat: Genesis 41

Poprzedni rozdział
Następny rozdział
YouVersion

Zachęcanie i wzywanie cię do codziennego szukania bliskości z Bogiem.

Misja

O YouVersion

Praca

Wolontariat

Blog

Prasa

Przydatne linki

Pomoc

Wesprzyj

Przekłady Biblii

Biblie audio

Języki Biblii

Werset dnia


Cyfrowa misja

Life.Church
Polski

©2026 Life.Church / YouVersion

Polityka prywatnościRegulamin
Program ujawniania luk w zabezpieczeniach
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest