1
Genesis 38:10
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Zimene ankachitazi zinayipira Yehova. Choncho anamulanganso ndi imfa.
Porównaj
Przeglądaj Genesis 38:10
2
Genesis 38:9
Koma Onani anadziwa kuti mwanayo sadzakhala wake. Choncho nthawi zonse pamene amagona naye mkaziyo, ankatayira umuna pansi kuti asamuberekere mwana mʼbale wake.
Przeglądaj Genesis 38:9