1
Genesis 30:22
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Kenaka, Mulungu anakumbukira Rakele namva pemphero lake ndi kulola kuti akhale ndi mwana.
Porównaj
Przeglądaj Genesis 30:22
2
Genesis 30:24
Iye anamutcha mwanayo Yosefe, ndipo anati, “Mulungu andipatsenso mwana wina.”
Przeglądaj Genesis 30:24
3
Genesis 30:23
Rakele anatenga pathupi nabala mwana wamwamuna ndipo anati, “Mulungu wandichotsera manyazi anga.”
Przeglądaj Genesis 30:23