Logo YouVersion
BibliaPlanyNagrania wideo
Pobierz aplikację
Wybór języka
Ikona wyszukiwania

Popularne wersety biblijne z Genesis 26

1

Genesis 26:3

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Khala mʼdziko lino ndipo ndidzakhala nawe ndi kukudalitsa. Pakuti kwa iwe ndi zidzukulu zako ndidzapereka mayiko onsewa. Choncho ndidzakwaniritsa pangano limene ndinalumbira kwa Abrahamu, abambo ako.

Porównaj

Przeglądaj Genesis 26:3

2

Genesis 26:4-5

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Zidzukulu zako ndidzazichulukitsa ngati nyenyezi za mu mlengalenga ndi kuzipatsa mayiko onsewa. Ndiponso anthu onse a pa dziko lapansi adzadalitsika kudzera mwa zidzukulu zako, chifukwa Abrahamu anandimvera, nasunga malamulo anga onse.”

Porównaj

Przeglądaj Genesis 26:4-5

3

Genesis 26:22

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Anachokapo pamenepo nakakumba china. Koma apa sanakanganiranenso ndi munthu. Iye anachitcha Kutakasuka, nati, “Tsopano Yehova watipatsa ife malo otakasukirako ndipo tilemera muno.”

Porównaj

Przeglądaj Genesis 26:22

4

Genesis 26:2

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yehova anadza kwa Isake nati, “Usapite ku Igupto; koma ukhale mʼdziko limene ndidzakuwuza kuti ukakhalemo.

Porównaj

Przeglądaj Genesis 26:2

5

Genesis 26:25

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Isake anamanga guwa lansembe pamenepo ndipo anapembedza Yehova. Pomwepo anamanga tenti yake, ndipo antchito ake anakumba chitsime.

Porównaj

Przeglądaj Genesis 26:25

Poprzedni rozdział
Następny rozdział
YouVersion

Zachęcanie i wzywanie cię do codziennego szukania bliskości z Bogiem.

Misja

O YouVersion

Praca

Wolontariat

Blog

Prasa

Przydatne linki

Pomoc

Wesprzyj

Przekłady Biblii

Biblie audio

Języki Biblii

Werset dnia


Cyfrowa misja

Life.Church
Polski

©2026 Life.Church / YouVersion

Polityka prywatnościRegulamin
Program ujawniania luk w zabezpieczeniach
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest