Logo YouVersion
BibliaPlanyNagrania wideo
Pobierz aplikację
Wybór języka
Ikona wyszukiwania

Popularne wersety biblijne z Eksodo 5

1

Eksodo 5:1

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Zitachitika izi, Mose ndi Aaroni anapita kwa Farao ndipo anati, “Yehova Mulungu wa Israeli akuti, ‘Aloleni anthu anga apite, kuti akachite chikondwerero cha Ine mʼchipululu.’ ”

Porównaj

Przeglądaj Eksodo 5:1

2

Eksodo 5:23

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Chipitireni changa kwa Farao kukamuyankhula mʼdzina lanu, iye wakhala akuzunza anthuwa, ndipo inu simunawapulumutse konse anthu anu.”

Porównaj

Przeglądaj Eksodo 5:23

3

Eksodo 5:22

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Mose anabwerera kwa Yehova ndipo anati, “Chonde Ambuye, chifukwa chiyani mukuzunza anthu anu? Kodi munanditumira zimenezi?

Porównaj

Przeglądaj Eksodo 5:22

4

Eksodo 5:2

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Koma Farao anati, “Yehova ndani kuti ine ndimumvere ndi kulola Aisraeli kuti apite? Ine Yehova sindikumudziwa ndipo sindilola kuti Aisraeli apite.”

Porównaj

Przeglądaj Eksodo 5:2

5

Eksodo 5:8-9

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Koma musawachepetsere chiwerengero cha njerwa chomwe munawalamulira kale kuti aziwumba. Iwowa ndi aulesi. Nʼchifukwa chake akulira kuti, ‘Tiloleni tipite tikapereke nsembe kwa Mulungu wathu.’ Muwakhawulitse ndi ntchito anthu amenewa kuti azitanganidwa, asakhale ndi mpata omvera zabodza.”

Porównaj

Przeglądaj Eksodo 5:8-9

Bezpłatne plany czytania i rozważania na temat: Eksodo 5

Poprzedni rozdział
Następny rozdział
YouVersion

Zachęcanie i wzywanie cię do codziennego szukania bliskości z Bogiem.

Misja

O YouVersion

Praca

Wolontariat

Blog

Prasa

Przydatne linki

Pomoc

Wesprzyj

Przekłady Biblii

Biblie audio

Języki Biblii

Werset dnia


Cyfrowa misja

Life.Church
Polski

©2026 Life.Church / YouVersion

Polityka prywatnościRegulamin
Program ujawniania luk w zabezpieczeniach
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest