1
EKSODO 25:8-9
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo andimangire malo opatulika; kuti ndikhale pakati pao. Monga mwa zonse Ine ndilikuonetsa iwe, chifaniziro cha Kachisi, ndi chifaniziro cha zipangizo zake zonse, momwemo uchimange.
ႏွိုင္းယွဥ္
EKSODO 25:8-9ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
EKSODO 25:2
Lankhula ndi ana a Israele, kuti anditengere chopereka; ulandire chopereka changa kwa munthu aliyense mtima wake umfunitsa mwini.
EKSODO 25:2ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား