1
EKSODO 24:17-18
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo maonekedwe a ulemerero wa Yehova anali ngati moto wonyeketsa pamwamba pa phiri, pamaso pa ana a Israele. Ndipo Mose analowa m'kati mwa mtambo, nakwera m'phirimo; ndipo Mose anakhala m'phiri masiku makumi anai usana ndi usiku.
ႏွိုင္းယွဥ္
EKSODO 24:17-18ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
EKSODO 24:16
Ndipo ulemerero wa Yehova unakhalabe pa phiri la Sinai, ndi mtambo unaliphimba masiku asanu ndi limodzi; ndipo tsiku lachisanu ndi chiwiri Iye ali m'kati mwa mtambo anaitana Mose.
EKSODO 24:16ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
3
EKSODO 24:12
Ndipo Yehova anati kwa Mose, Ukwere kudza kwa Ine m'phiri muno, nukhale pompano; ndipo ndidzakupatsa magome amiyala, ndi chilamulo ndi malamulo ndawalembera kuti uwalangize.
EKSODO 24:12ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား