1
Maluko 7:21-23
Nyanja
NTNYBL2025
Pakuti kuchokela mmitima ya wandhu, yachoka maganizo yoipa ni chigololo ni unghungu ni kupha, uhule ni khumbilo lo funa chuma chambili ni voipa ni unami ni kukafula ni khumbilo lofuna chigololo ni mbwinya ni usabwabwa. Voipa vimenevo vichoka mkati mwa wandhu, navo vimchita mundhu siwadavomelezeka kumlambila Mnungu.”
താരതമ്യം
Maluko 7:21-23 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
Maluko 7:15
Palibe chindhu chilowa mkati mwa mundhu kuchokela kubwalo icho chikhoza kumchita siwadavomelezeka kwa kumlambila Mnungu. Nambho icho chichoka mkati mwa mundhu ndeicho chimchita mundhu siwadavomelezeka kwa kumlambila Mnungu.
Maluko 7:15 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
Maluko 7:6
Yesu wadaayangha, “Agunghuli anyiimwe, mlosi Isaya wadakuloselani bwino anyiimwe, yapo wadalemba, ‘Mnungu wakamba, wandhu anyiawa anilimekeza kwa milomo yaope, nambho mitima yao, ilikutali niine.
Maluko 7:6 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
Maluko 7:7
Ni kunilambila kwawo sikufunika, pakuti ayaluza mayaluzo ya wandhupe ngati mayaluzo ya Mnungu.’”
Maluko 7:7 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
Maluko 7:8
“Anyiimwe muyasiya malamulo ya Mnungu ni kuchata chikhalidwe cha wandhu.”
Maluko 7:8 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ