1
GENESIS 41:16
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo Yosefe anayankha Farao kuti, Si mwa ine; koma Mulungu adzayankha Farao mwamtendere.
താരതമ്യം
GENESIS 41:16 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
GENESIS 41:38
Ndipo Farao anati kwa anyamata ake, Kodi ife tidzaone munthu ngati uyu, mzimu wa Mulungu uli m'mtima mwake?
GENESIS 41:38 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
GENESIS 41:39-40
Ndipo Farao anati kwa Yosefe, Popeza Mulungu wakuonetsa iwe zonsezo palibe wina wakuzindikira ndi wanzeru ngati iwe. Uziyang'anira pa nyumba yanga, ndipo anthu anga onse adzalamulidwa mwa mau ako; pa mpando wachifumu pokha ine ndidzakuposa iwe.
GENESIS 41:39-40 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
GENESIS 41:52
Ndipo dzina la wachiwiri anamutcha Efuremu: chifukwa Mulungu anandibalitsa ine m'dziko la kusauka kwanga.
GENESIS 41:52 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
GENESIS 41:51
Ndipo Yosefe anamutcha dzina la woyamba Manase, chifukwa anati iye, Mulungu wandiiwalitsa ine zovuta zanga zonse, ndi nyumba yonse ya atate wanga.
GENESIS 41:51 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ