1
MACHITIDWE A ATUMWI 4:12
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo palibe chipulumutso mwa wina yense, pakuti palibe dzina lina pansi pa thambo la kumwamba, lopatsidwa mwa anthu, limene tiyenera kupulumutsidwa nalo.
താരതമ്യം
MACHITIDWE A ATUMWI 4:12 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MACHITIDWE A ATUMWI 4:31
Ndipo m'mene adapemphera iwo, panagwedezeka pamalo pamene adasonkhanirapo; ndipo anadzazidwa onse ndi Mzimu Woyera, nalankhula mau a Mulungu molimbika mtima.
MACHITIDWE A ATUMWI 4:31 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MACHITIDWE A ATUMWI 4:29
Ndipo tsopano Ambuye, penyani mau ao akuopsa, ndipo patsani kwa akapolo anu alankhule mau anu ndi kulimbika mtima konse
MACHITIDWE A ATUMWI 4:29 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MACHITIDWE A ATUMWI 4:11
Iye ndiye mwalawo woyesedwa wopanda pake ndi inu omanga nyumba, umene unayesedwa mutu wa pangodya.
MACHITIDWE A ATUMWI 4:11 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MACHITIDWE A ATUMWI 4:13
Koma pakuona kulimbika mtima kwa Petro ndi Yohane, ndipo pozindikira kuti ndiwo anthu osaphunzira ndi opulukira, anazizwa ndipo anawazindikira, kuti adakhala pamodzi ndi Yesu.
MACHITIDWE A ATUMWI 4:13 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
MACHITIDWE A ATUMWI 4:32
Ndipo unyinji wa iwo akukhulupirira anali wa mtima umodzi ndi moyo umodzi; ndipo sananena mmodzi kuti kanthu ka chuma anali nacho ndi kake ka iye yekha; koma anali nazo zonse zodyerana.
MACHITIDWE A ATUMWI 4:32 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ