YouVersion logotips
Meklēt ikonu

Genesis 3:6

Genesis 3:6 CCL

Pamene mkaziyo anaona kuti mtengowo unali wabwino kudya ndi wokongola ndi kuti unali wopatsa nzeru, anatengako zipatso zake nadya. Zina anamupatsako mwamuna wake amene anali naye pomwepo ndipo naye anadyanso.

Bezmaksas lasīšanas plāni un pārdomas par tēmu Genesis 3:6