YouVersion logó
BibliaOlvasótervekVideók
Szerezd meg az alkalmazást
Nyelvválasztó
Keresés

Népszerű bibliai igeversek innen: Gen. 2

1

Gen. 2:24

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Nchifukwa chake mwamuna amasiya atate ndi amai, ndipo amaphatikana ndi mkazi wake, choncho aŵiriwo amakhala thupi limodzi.

Összehasonlít

Fedezd fel: Gen. 2:24

2

Gen. 2:18

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Pambuyo pake Chauta adati, “Sibwino kuti munthuyu akhale yekha. Ndipanga mnzake woti azimthandiza.”

Összehasonlít

Fedezd fel: Gen. 2:18

3

Gen. 2:7

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Tsono Chauta adatenga dothi pa nthaka, ndipo adaumba munthu ndi dothilo. Adamuuzira mpweya wopatsa moyo m'mphuno zake, ndipo munthuyo adakhala wamoyo.

Összehasonlít

Fedezd fel: Gen. 2:7

4

Gen. 2:23

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Adamu adati, “Uyutu ndiye ndi fupa lochokera ku mafupa anga, mnofu wochokera ku mnofu wanga. Adzatchedwa Mkazi, chifukwa watengedwa kwa Mwamuna.”

Összehasonlít

Fedezd fel: Gen. 2:23

5

Gen. 2:3

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Mulungu adadalitsa tsiku lachisanu ndi chiŵirilo, naliyeretsa, chifukwa choti pa tsiku limenelo adapuma atatsiriza zonse zimene ankachita.

Összehasonlít

Fedezd fel: Gen. 2:3

6

Gen. 2:25

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Mwamunayo ndi mkazi wake uja, onse anali maliseche, komabe sankachita manyazi.

Összehasonlít

Fedezd fel: Gen. 2:25

Előző fejezet
Következő fejezet
YouVersion

Bátorítás és kihívás arra, hogy minden nap keressük az Istennel való bensőséges kapcsolatot.

Misszió

Rólunk

Álláslehetőség

Önkéntesség

Blog

Sajtó

Hasznos linkek

Súgó

Adomány

Biblia-fordítások

Hangos Bibliák

Biblia nyelve

Napi igevers


Egy digitális misszió:

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Adatvédelmi irányelvekÁSZF
Felelős közzététel
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Kezdőoldal

Biblia

Olvasótervek

Videók