YouVersion logó
BibliaOlvasótervekVideók
Szerezd meg az alkalmazást
Nyelvválasztó
Keresés

Népszerű bibliai igeversek innen: Genesis 2

1

Genesis 2:24

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Nʼchifukwa chake, mwamuna amasiya abambo ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake ndipo awiriwo amakhala thupi limodzi.

Összehasonlít

Fedezd fel: Genesis 2:24

2

Genesis 2:18

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Yehova Mulungu anati, “Sibwino kuti munthu akhale yekha. Ndidzamupangira mnzake womuthandiza.”

Összehasonlít

Fedezd fel: Genesis 2:18

3

Genesis 2:7

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Tsono Yehova Mulungu anawumba munthu kuchokera ku dothi nawuziramo mpweya wamoyo mʼmphuno mwake ndipo munthuyo anakhala wamoyo.

Összehasonlít

Fedezd fel: Genesis 2:7

4

Genesis 2:23

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Munthu uja anati, “Uyu ndiye fupa lochokera ku mafupa anga ndi mnofu wochokera ku mnofu wanga; adzatchedwa ‘mkazi,’ popeza wachokera mwa mwamuna.”

Összehasonlít

Fedezd fel: Genesis 2:23

5

Genesis 2:3

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Mulungu anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri nalipatula, chifukwa pa tsiku limeneli Iye anapumula ku ntchito yonse yolenga imene anayigwira.

Összehasonlít

Fedezd fel: Genesis 2:3

6

Genesis 2:25

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Munthu uja ndi mkazi wakeyo, onse awiri anali maliseche ndipo analibe manyazi.

Összehasonlít

Fedezd fel: Genesis 2:25

Előző fejezet
Következő fejezet
YouVersion

Bátorítás és kihívás arra, hogy minden nap keressük az Istennel való bensőséges kapcsolatot.

Misszió

Rólunk

Álláslehetőség

Önkéntesség

Blog

Sajtó

Hasznos linkek

Súgó

Adomány

Biblia-fordítások

Hangos Bibliák

Biblia nyelve

Napi igevers


Egy digitális misszió:

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Adatvédelmi irányelvekÁSZF
Felelős közzététel
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Kezdőoldal

Biblia

Olvasótervek

Videók