YouVersion logó
BibliaOlvasótervekVideók
Szerezd meg az alkalmazást
Nyelvválasztó
Keresés

Népszerű bibliai igeversek innen: GENESIS 11

1

GENESIS 11:6-7

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anati, Taonani, anthu ali amodzi, ndipo onse ali nacho chinenedwe chao chimodzi; ndipo ichi ayamba kuchita: ndipo tsopano palibe kanthu kakuletsedwa nao kamene akafuna kuchita. Tiyeni, titsike, pomwepo tisokoneze chinenedwe chao, kuti wina asamvere chinenedwe cha mnzake.

Összehasonlít

Fedezd fel: GENESIS 11:6-7

2

GENESIS 11:4

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anati, Tiyeni, timange mzinda ndi nsanja, pamutu pake pafikire kumwamba; ndipo tidzipangire ife tokha dzina kuti tisabalalike padziko lonse lapansi.

Összehasonlít

Fedezd fel: GENESIS 11:4

3

GENESIS 11:9

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chifukwa chake anatcha dzina lake Babiloni pakuti kumeneko Yehova anasokoneza chinenedwe cha dziko lonse lapansi; kuyambira pamenepo Yehova anabalalitsa iwo padziko lonse lapansi.

Összehasonlít

Fedezd fel: GENESIS 11:9

4

GENESIS 11:1

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo dziko lapansi linali la chinenedwe chimodzi ndi chilankhulidwe chimodzi.

Összehasonlít

Fedezd fel: GENESIS 11:1

5

GENESIS 11:5

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anatsikira kudzaona mzinda ndi nsanja imene analinkumanga ana a anthu.

Összehasonlít

Fedezd fel: GENESIS 11:5

6

GENESIS 11:8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anabalalitsa iwo padziko lonse lapansi, ndipo analeka kumanga mzinda.

Összehasonlít

Fedezd fel: GENESIS 11:8

Előző fejezet
Következő fejezet
YouVersion

Bátorítás és kihívás arra, hogy minden nap keressük az Istennel való bensőséges kapcsolatot.

Misszió

Rólunk

Álláslehetőség

Önkéntesség

Blog

Sajtó

Hasznos linkek

Súgó

Adomány

Biblia-fordítások

Hangos Bibliák

Biblia nyelve

Napi igevers


Egy digitális misszió:

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Adatvédelmi irányelvekÁSZF
Felelős közzététel
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Kezdőoldal

Biblia

Olvasótervek

Videók