Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan LUKA 24

1

LUKA 24:49

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo onani, Ine nditumiza pa inu lonjezano la Atate wanga; koma khalani inu m'mudzi muno, kufikira mwavekedwa ndi mphamvu yochokera Kumwamba.

Konpare

Eksplore LUKA 24:49

2

LUKA 24:6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Palibe kuno Iye, komatu anauka; kumbukirani muja adalankhula nanu, pamene analinso m'Galileya

Konpare

Eksplore LUKA 24:6

3

LUKA 24:31-32

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo maso ao anatseguka, ndipo anamzindikira Iye; ndipo anawakanganukira Iye, nawachokera. Ndipo anati wina kwa mnzake, Mtima wathu sunali wotentha m'kati mwathu nanga m'mene analankhula nafe m'njira, m'mene anatitsegulira malembo?

Konpare

Eksplore LUKA 24:31-32

4

LUKA 24:46-47

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo anati kwa iwo, Kotero kwalembedwa, kuti Khristu amve zowawa, nauke kwa akufa tsiku lachitatu; ndi kuti kulalikidwe m'dzina lake kulapa ndi kukhululukidwa kwa machimo kwa mitundu yonse, kuyambira ku Yerusalemu.

Konpare

Eksplore LUKA 24:46-47

5

LUKA 24:2-3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anapeza mwala unakunkhunizidwa kuuchotsa pamanda. Ndipo m'mene analowa sanapeze mtembo wa Ambuye Yesu.

Konpare

Eksplore LUKA 24:2-3

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak LUKA 24

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo