Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan LUKA 19

1

LUKA 19:10

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakuti Mwana wa Munthu anadza kufunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.

Konpare

Eksplore LUKA 19:10

2

LUKA 19:38

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

nanena, Wolemekezeka Mfumuyo ikudza m'dzina la Ambuye; mtendere m'Mwamba, ndi ulemerero m'Mwambamwamba.

Konpare

Eksplore LUKA 19:38

3

LUKA 19:9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yesu anati kwa iye, Lero chipulumutso chagwera nyumba iyi, popeza iyenso ndiye mwana wa Abrahamu.

Konpare

Eksplore LUKA 19:9

4

LUKA 19:5-6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo m'mene anadza pamalopo Yesu anakweza maso nati kwa iye, Zakeyo, fulumira, nutsike; pakuti lero ndiyenera kukhala m'nyumba mwako. Ndipo anafulumira, natsika, namlandira Iye wokondwera.

Konpare

Eksplore LUKA 19:5-6

5

LUKA 19:8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Zakeyo anaimirira nati kwa Ambuye, Taonani, Ambuye, gawo limodzi la zanga zonse zogawika pakati ndipatsa osauka; ndipo ngati ndalanda kanthu kwa munthu monyenga, ndimbwezera kanai.

Konpare

Eksplore LUKA 19:8

6

LUKA 19:39-40

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Afarisi ena a m'khamu la anthu anati kwa Iye, Mphunzitsi, dzudzulani ophunzira anu. Ndipo anayankha nati, Ndinena ndi inu, ngati awa khala chete miyala idzafuula.

Konpare

Eksplore LUKA 19:39-40

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak LUKA 19

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo