1
YOHANE 13:34-35
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndikupatsani inu lamulo latsopano, kuti mukondane wina ndi mnzake; monga ndakonda inu, kuti inunso mukondane wina ndi mnzake. Mwa ichi adzazindikira onse kuti muli ophunzira anga, ngati muli nacho chikondano wina ndi mnzake.
Konpare
Eksplore YOHANE 13:34-35
2
YOHANE 13:14-15
Chifukwa chake, ngati Ine Ambuye ndi Mphunzitsi, ndasambitsa mapazi anu, inunso muyenera kusambitsana mapazi wina ndi mnzake. Pakuti ndakupatsani inu chitsanzo, kuti, monga Ine ndakuchitirani inu, inunso muchite.
Eksplore YOHANE 13:14-15
3
YOHANE 13:7
Yesu anayankha nati kwa iye, Chimene ndichita Ine suchidziwa tsopano; koma udzadziwa m'tsogolo mwake.
Eksplore YOHANE 13:7
4
YOHANE 13:16
Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Kapolo sali wamkulu ndi mbuye wake; kapena mtumwi sali wamkulu ndi womtuma iye.
Eksplore YOHANE 13:16
5
YOHANE 13:17
Ngati mudziwa izi, odala inu ngati muzichita.
Eksplore YOHANE 13:17
6
YOHANE 13:4-5
ananyamuka pamgonero, navula malaya ake; ndipo m'mene adatenga chopukutira, anadzimanga m'chuuno. Pomwepo anathira madzi m'nsambidwe, nayamba kusambitsa mapazi a ophunzira ake, ndi kuwapukuta ndi chopukutira, chimene anadzimanga nacho.
Eksplore YOHANE 13:4-5
Akèy
Bib
Plan yo
Videyo