Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan GENESIS 11

1

GENESIS 11:6-7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anati, Taonani, anthu ali amodzi, ndipo onse ali nacho chinenedwe chao chimodzi; ndipo ichi ayamba kuchita: ndipo tsopano palibe kanthu kakuletsedwa nao kamene akafuna kuchita. Tiyeni, titsike, pomwepo tisokoneze chinenedwe chao, kuti wina asamvere chinenedwe cha mnzake.

Konpare

Eksplore GENESIS 11:6-7

2

GENESIS 11:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati, Tiyeni, timange mudzi ndi nsanja, pamutu pake pafikire kumwamba; ndipo tidzipangire ife tokha dzina kuti tisabalalike pa dziko lonse lapansi.

Konpare

Eksplore GENESIS 11:4

3

GENESIS 11:9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chake anatcha dzina lake Babele; pakuti kumeneko Yehova anasokoneza chinenedwe cha dziko lonse lapansi; kuyambira pamenepo Yehova anabalalitsa iwo pa dziko lonse lapansi.

Konpare

Eksplore GENESIS 11:9

4

GENESIS 11:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo dziko lapansi linali la chinenedwe chimodzi ndi chilankhulidwe chimodzi.

Konpare

Eksplore GENESIS 11:1

5

GENESIS 11:5

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anatsikira kudzaona mudzi ndi nsanja imene analinkumanga ana a anthu.

Konpare

Eksplore GENESIS 11:5

6

GENESIS 11:8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anabalalitsa iwo pa dziko lonse lapansi, ndipo analeka kumanga mudzi.

Konpare

Eksplore GENESIS 11:8

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo