Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan MACHITIDWE A ATUMWI 5

1

MACHITIDWE A ATUMWI 5:29

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anayankha Petro ndi atumwi, nati, Tiyenera kumvera Mulungu koposa anthu.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 5:29

2

MACHITIDWE A ATUMWI 5:42

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo masiku onse, m'Kachisi ndi m'nyumba, sanaleka kuphunzitsa ndi kulalikira Khristu Yesu.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 5:42

3

MACHITIDWE A ATUMWI 5:3-5

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma Petro anati, Ananiya, Satana anadzaza mtima wako chifukwa ninji kudzanyenga Mzimu Woyera, ndi kupatula pa mtengo wake wa mundawo? Pamene unali nao, sunali wako kodi? Ndipo pamene unagulitsa sunali m'manja mwako kodi? Bwanji chinalowa ichi mumtima mwako? Sunanyenga anthu, komatu Mulungu. Koma Ananiya pakumva mau awa anagwa pansi namwalira: ndipo mantha akulu anagwera onse akumvawo.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 5:3-5

4

MACHITIDWE A ATUMWI 5:38-39

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo tsopano ndinena ndi inu, Lekani anthu amenewa, nimuwalole akhale; pakuti ngati uphungu umene kapena ntchito iyi ichokera kwa anthu, idzapasuka; koma ngati ichokera kwa Mulungu simungathe kuwapasula; kuti kapena mungapezeke otsutsana ndi Mulungu.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 5:38-39

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak MACHITIDWE A ATUMWI 5

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo