Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan MACHITIDWE A ATUMWI 3

1

MACHITIDWE A ATUMWI 3:19

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chake lapani, bwererani kuti afafanizidwe machimo anu, kotero kuti zidze nyengo zakutsitsimutsa zochokera kunkhope ya Ambuye

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 3:19

2

MACHITIDWE A ATUMWI 3:6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma Petro anati, Siliva ndi golide ndilibe; koma chimene ndili nacho, ichi ndikupatsa, M'dzina la Yesu Khristu Mnazarayo, yenda.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 3:6

3

MACHITIDWE A ATUMWI 3:7-8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anamgwira iye kudzanja lake lamanja, namnyamutsa; ndipo pomwepo mapazi ake ndi mfundo za kumapazi zinalimbikitsidwa. Ndipo anazunzuka, naimirira, nayenda; ndipo analowa pamodzi nao m'Kachisi, nayenda, nalumpha, nayamika Mulungu.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 3:7-8

4

MACHITIDWE A ATUMWI 3:16

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pa chikhulupiriro cha m'dzina lake dzina lakelo linalimbikitsa iye amene mumuona, nimumdziwa; ndipo chikhulupiriro chili mwa Iye chinampatsa kuchira konse kumeneku pamaso pa inu nonse.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 3:16

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak MACHITIDWE A ATUMWI 3

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo