Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan MACHITIDWE A ATUMWI 20

1

MACHITIDWE A ATUMWI 20:35

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

M'zinthu zonse ndinakupatsani chitsanzo, chakuti pogwiritsa ntchito, kotero muyenera kuthandiza ofooka ndi kukumbuka mau a Ambuye Yesu, kuti anati yekha, Kupatsa kutidalitsa koposa kulandira.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 20:35

2

MACHITIDWE A ATUMWI 20:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Komatu sindiuyesa kanthu moyo wanga, kuti uli wa mtengo wake kwa ine ndekha; kotero kuti ndikatsirize njira yanga, ndi utumiki ndinaulandira kwa Ambuye Yesu, kuchitira umboni Uthenga Wabwino wa chisomo cha Mulungu.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 20:24

3

MACHITIDWE A ATUMWI 20:28

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Tadzichenjerani nokha, ndi gulu lonse, pamenepo Mzimu Woyera anakuikani oyang'anira, kuti muwete Mpingo wa Mulungu, umene anaugula ndi mwazi wa Iye yekha.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 20:28

4

MACHITIDWE A ATUMWI 20:32

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo tsopano ndikuikizani kwa Mulungu, ndi kwa mau a chisomo chake, chimene chili ndi mphamvu yakumangirira ndi kupatsa inu cholowa mwa onse oyeretsedwa.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 20:32

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak MACHITIDWE A ATUMWI 20

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo