Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan MACHITIDWE A ATUMWI 17

1

MACHITIDWE A ATUMWI 17:27

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

kuti afunefune Mulungu, kapena akamfufuze ndi kumpeza, ngakhale sakhala patali ndi yense wa ife

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 17:27

2

MACHITIDWE A ATUMWI 17:26

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo ndi mmodzi analenga mitundu yonse ya anthu, kuti akhale ponse pa nkhope ya dziko lapansi, atapangiratu nyengo zao, ndi malekezero a pokhala pao

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 17:26

3

MACHITIDWE A ATUMWI 17:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Mulungu amene analenga dziko lapansi ndi zonse zili momwemo, Iyeyo, ndiye mwini kumwamba ndi dziko lapansi, sakhala m'nyumba za kachisi zomangidwa ndi manja

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 17:24

4

MACHITIDWE A ATUMWI 17:31

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

chifukwa anapangira tsiku limene adzaweruza dziko lokhalamo anthu m'chilungamo, ndi munthu amene anamuikiratu; napatsa anthu onse chitsimikizo, pamene anamuukitsa Iye kwa akufa.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 17:31

5

MACHITIDWE A ATUMWI 17:29

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Popeza tsono tili mbadwa za Mulungu, sitiyenera kulingalira kuti umulungu uli wofanafana ndi golide, kapena siliva, kapena mwala, wolocha ndi luso ndi zolingalira za anthu.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 17:29

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak MACHITIDWE A ATUMWI 17

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo