Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan MACHITIDWE A ATUMWI 14

1

MACHITIDWE A ATUMWI 14:15

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

nafuula nati, Anthuni, bwanji muchita zimenezi? Ifenso tili anthu a mkhalidwe wathu umodzimodzi ndi wanu, akulalikira kwa inu Uthenga Wabwino, wakuti musiye zinthu zachabe izi, nimutembenukire kwa Mulungu wamoyo, amene analenga zakumwamba ndi zapansi, ndi nyanja, ndi zonse zili momwemo

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 14:15

2

MACHITIDWE A ATUMWI 14:9-10

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ameneyo anamva Paulo alinkulankhula; ndipo Paulo pomyang'anitsa, ndi kuona kuti anali ndi chikhulupiriro cholandira nacho moyo, anati ndi mau akulu, Taimirira. Ndipo iyeyu anazunzuka, nayenda.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 14:9-10

3

MACHITIDWE A ATUMWI 14:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pamene anawaikira akulu mosankha mu Mpingo uliwonse, ndi kupemphera pamodzi ndi kusala kudya, naikiza iwo kwa Ambuye amene anamkhulupirirayo.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 14:23

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak MACHITIDWE A ATUMWI 14

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo