Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan MACHITIDWE A ATUMWI 13

1

MACHITIDWE A ATUMWI 13:2-3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pa kutumikira Ambuye iwowa, ndi kusala chakudya, Mzimu Woyera anati, Mundipatulire Ine Barnabasi ndi Saulo ku ntchito imene ndinawaitanirako. Pamenepo, m'mene adasala chakudya ndi kupemphera ndi kuika manja pa iwo, anawatumiza amuke.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 13:2-3

2

MACHITIDWE A ATUMWI 13:39

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo mwa Iye yense wokhulupirira ayesedwa wolungama kumchotsera zonse zimene simunangathe kudzichotsera poyesedwa wolungama ndi chilamulo cha Mose.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 13:39

3

MACHITIDWE A ATUMWI 13:47

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakuti kotero anatilamula Ambuye ndi kuti, Ndakuika iwe kuunika kwa amitundu, kuti udzakhala iwe chipulumutso kufikira malekezero a dziko.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 13:47

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak MACHITIDWE A ATUMWI 13

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo