YouVersion-logo
RaamattuSuunnitelmatVideot
Hanki sovellus
Kielen valitsin
Hakukuvake

Suosittuja jakeita Raamatun kirjasta Gen. 2

1

Gen. 2:24

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Nchifukwa chake mwamuna amasiya atate ndi amai, ndipo amaphatikana ndi mkazi wake, choncho aŵiriwo amakhala thupi limodzi.

Vertaa

Tutki Gen. 2:24

2

Gen. 2:18

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Pambuyo pake Chauta adati, “Sibwino kuti munthuyu akhale yekha. Ndipanga mnzake woti azimthandiza.”

Vertaa

Tutki Gen. 2:18

3

Gen. 2:7

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Tsono Chauta adatenga dothi pa nthaka, ndipo adaumba munthu ndi dothilo. Adamuuzira mpweya wopatsa moyo m'mphuno zake, ndipo munthuyo adakhala wamoyo.

Vertaa

Tutki Gen. 2:7

4

Gen. 2:23

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Adamu adati, “Uyutu ndiye ndi fupa lochokera ku mafupa anga, mnofu wochokera ku mnofu wanga. Adzatchedwa Mkazi, chifukwa watengedwa kwa Mwamuna.”

Vertaa

Tutki Gen. 2:23

5

Gen. 2:3

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Mulungu adadalitsa tsiku lachisanu ndi chiŵirilo, naliyeretsa, chifukwa choti pa tsiku limenelo adapuma atatsiriza zonse zimene ankachita.

Vertaa

Tutki Gen. 2:3

6

Gen. 2:25

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Mwamunayo ndi mkazi wake uja, onse anali maliseche, komabe sankachita manyazi.

Vertaa

Tutki Gen. 2:25

Edellinen luku
Seuraava luku
YouVersion

Rohkaisemassa ja haastamassa sinua etsimään läheisyyttä Jumalan kanssa joka päivä.

Palvelutehtävä

Tietoa

Uramahdollisuudet

Vapaaehtoiseksi

Blogi

Lehdistö

Hyödyllisiä linkkejä

Apua

Lahjoita

Raamatunkäännökset

Ääniraamatut

Kielet

Päivän jae


Digitaalinen palvelutehtävä

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

YksityisyyskäytännötKäyttöehdot
Haavoittuvuuden paljastamisohjelma
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Koti

Raamattu

Suunnitelmat

Videot