Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

Matayo 20:26-28

Matayo 20:26-28 NTNYBL2025

Anyiimwe musadachita chimwecho, mmalo mwake, waliyonjhe uyo wafuna kukhala wamkulu pakati panu, wafunika wakhale mbowa wa wonjhe. Waliyonjhe uyo wafuna kukhala woyamba pakati panu wakhale mbowa wa wonjhe. Ngati umo ili kwa Mwana wa Mundhu siwadajhe kutumikilidwa, nambho kutumikila ni kuuchocha umoyo wake kwa kwaombola wandhu ambili.”

Lee Matayo 20

Planes de lectura y devocionales gratis relacionados con Matayo 20:26-28