ZEKARIYA Mau Oyamba
Mau Oyamba
Bukuli lili ndi zigawo ziwiri: Gawo loyamba ndi mau amene mneneri adalalikira kuyambira chaka cha 520 BC. Zekariya akulongosola zimene adaziwona m'masomphenya ndipo akuwachenjeza anthuwo nawalimbitsa mtima kuti akonzenso Kachisi komanso mzinda wa Yerusalemu. Iwo ayenera adziyeretsa popeza Yehova adzawadalitsa (1—8). Gawo lachiwiri ndi kaundula wa mauneneri osiyanasiyana onena za kubwera kwa Mesiya ndipo tsiku la chiweruzo (9—14).
Za mkatimu
Mau oyamba 1.1—8.23
Mau a Yehova aimba mlandu mitundu ina ya anthu 9.1-8
Mau ena olonjeza zabwino 9.9—14.21
Actualmente seleccionado:
ZEKARIYA Mau Oyamba: BLPB2014
Destacar
Compartir
Copiar
¿Quieres tener guardados todos tus destacados en todos tus dispositivos? Regístrate o inicia sesión
The Bible in Chichewa Published as Buku Lopatulika
Bible Society of Malawi
ZEKARIYA Mau Oyamba
Mau Oyamba
Bukuli lili ndi zigawo ziwiri: Gawo loyamba ndi mau amene mneneri adalalikira kuyambira chaka cha 520 BC. Zekariya akulongosola zimene adaziwona m'masomphenya ndipo akuwachenjeza anthuwo nawalimbitsa mtima kuti akonzenso Kachisi komanso mzinda wa Yerusalemu. Iwo ayenera adziyeretsa popeza Yehova adzawadalitsa (1—8). Gawo lachiwiri ndi kaundula wa mauneneri osiyanasiyana onena za kubwera kwa Mesiya ndipo tsiku la chiweruzo (9—14).
Za mkatimu
Mau oyamba 1.1—8.23
Mau a Yehova aimba mlandu mitundu ina ya anthu 9.1-8
Mau ena olonjeza zabwino 9.9—14.21
Actualmente seleccionado:
:
Destacar
Compartir
Copiar
¿Quieres tener guardados todos tus destacados en todos tus dispositivos? Regístrate o inicia sesión
The Bible in Chichewa Published as Buku Lopatulika
Bible Society of Malawi