Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

AROMA 12:4-5

AROMA 12:4-5 BLPB2014

Pakuti monga m'thupi limodzi tili nazo ziwalo zambiri, ndipo ziwalo zonsezo sizili nayo ntchito imodzimodzi; chomwecho ife, ndife ambiri, tili thupi limodzi mwa Khristu, ndi ziwalo zinzake, wina ndi wina.

Planes de lectura y devocionales gratis relacionados con AROMA 12:4-5