Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

MARKO 5:35-36

MARKO 5:35-36 BLPB2014

M'mene iye ali chilankhulire, anafika a kunyumba ya mkulu wa sunagoge, nanena, kuti, Mwana wako wafa; uvutiranjinso Mphunzitsi? Koma Yesu wosasamala mau olankhulidwawo, ananena kwa mkulu wa sunagoge, Usaope, khulupirira kokha.

Planes de lectura y devocionales gratis relacionados con MARKO 5:35-36