Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

MATEYU 6:19-21

MATEYU 6:19-21 BLPB2014

Musadzikundikire nokha chuma pa dziko lapansi, pamene njenjete ndi dzimbiri ziononga; ndi pamene mbala ziboola ndi kuba: koma mudzikundikire nokha chuma m'Mwamba, pamene njenjete kapena dzimbiri siziononga, ndipo mbala siziboola ndi kuba; pakuti kumene kuli chuma chako, komwe udzakhala mtima wakonso.

Planes de lectura y devocionales gratis relacionados con MATEYU 6:19-21