Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

MATEYU 4:1-2

MATEYU 4:1-2 BLPB2014

Pamenepo Yesu anatengedwa ndi Mzimu kunka kuchipululu kukayesedwa ndi mdierekezi. Ndipo pamene Iye analibe kudya masiku makumi anai usana ndi usiku, pambuyo pake anamva njala.