Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

MATEYU 27:22-23

MATEYU 27:22-23 BLPB2014

Pilato ananena kwa iwo, Nanga ndidzachita chiyani ndi Yesu, wotchedwa Khristu? Onse anati, Apachikidwe pamtanda. Ndipo iye anati, Chifukwa ninji? Anachita choipa chotani? Koma iwo anafuulitsa kopambana, Apachikidwe pamtanda.

Planes de lectura y devocionales gratis relacionados con MATEYU 27:22-23