Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

MATEYU 14:16-17

MATEYU 14:16-17 BLPB2014

Koma Yesu anati kwa iwo, Iwo alibe chifukwa cha kumukira, apatseni ndinu adye. Koma iwo ananena kwa Iye, Ife tilibe kanthu pano koma mikate isanu, ndi nsomba ziwiri.