Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

MATEYU 10:32-33

MATEYU 10:32-33 BLPB2014

Chifukwa chake yense amene adzavomereza Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzamvomereza iye pamaso pa Atate wanga wa Kumwamba. Koma yense amene adzandikana Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzamkana iye pamaso pa Atate wanga wa Kumwamba.

Planes de lectura y devocionales gratis relacionados con MATEYU 10:32-33