Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

MALAKI 3:10

MALAKI 3:10 BLPB2014

Mubwere nalo limodzilimodzi lonse la khumi, kunyumba yosungiramo, kuti m'nyumba mwanga mukhale chakudya; ndipo mundiyese nako tsono, ati Yehova wa makamu, ngati sindikutsegulirani mazenera a kumwamba, ndi kukutsanulirani mdalitso wakuti adzasoweka malo akuulandira.

Planes de lectura y devocionales gratis relacionados con MALAKI 3:10