Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

MACHITIDWE A ATUMWI 11:23-24

MACHITIDWE A ATUMWI 11:23-24 BLPB2014

ameneyo, m'mene anafika, naona chisomo cha Mulungu, anakondwa; ndipo anawadandaulira onse, kuti atsimikize mtima kukhalabe ndi Ambuye; chifukwa anali munthu wabwino, ndi wodzala ndi Mzimu Woyera ndi chikhulupiriro: ndipo khamu lalikulu lidaonjezeka kwa Ambuye.

Planes de lectura y devocionales gratis relacionados con MACHITIDWE A ATUMWI 11:23-24