Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

2 AKORINTO 4:16-17

2 AKORINTO 4:16-17 BLPB2014

Chifukwa chake sitifooka; koma ungakhale umunthu wathu wakunja uvunda, wa m'kati mwathu ukonzedwa kwatsopano tsiku ndi tsiku. Pakuti chisautso chathu chopepuka cha kanthawi chitichitira ife kulemera koposa kwakukulu ndi kosatha kwa ulemerero