1
Maluko 1:35
Nyanja
NTNYBL2025
Umawamawa siku lidachatila, Yesu wadapita kubwalo kwa mujhi, pamalo yapo padalibe wandhu, kumeneko wadampembha Mnungu.
Comparar
Explorar Maluko 1:35
2
Maluko 1:15
Wadakamba, “Nyengo ya Mnungu yakwana yolamulila wandhu. Lapani ni kukhulupilila Uthenga Wabwino.”
Explorar Maluko 1:15
3
Maluko 1:10-11
Yesu yapo wadachuuka mmajhi, pamwepo wadaona kumwamba kwamasulidwa, ni Mzimu Woyela udamchikila ngati nghunda. Mvekelo wa Mnungu udaveka kuchokela kumwamba, niukamba, “Iwe nde mwana wanga uyo nikukonda, nikondelechedwa ni iwe.”
Explorar Maluko 1:10-11
4
Maluko 1:8
Ine nikubatizani kwa majhi, nambho iye siwakubatizeni kwa Mzimu Woyela.”
Explorar Maluko 1:8
5
Maluko 1:17-18
Yesu wadaakambila, “Nichateni, nane sinikuyaluzeni mukhale owapeleka wandhu kwa ine, ngati umo mmavuwila njhomba.” Pampajha adavisia vilepa vao nikumchata.
Explorar Maluko 1:17-18
6
Maluko 1:22
Wandhu yawo adamvela mayaluzo yake, adazizwa ndande siwamayaluze ngati umo amayaluzila oyaluza athauko la Musa, nambho iye wamayaluza ngati mundhu wa ulamulilo.
Explorar Maluko 1:22
Inicio
Biblia
Planes
Vídeos