1
MARKO 15:34
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo pa ora lachisanu ndi chinai Yesu anafuula ndi mau okweza, Eloi, Eloi, lama sabakitani? ndiko kusandulika, Mulungu wanga, Mulungu wanga mwandisiyiranji Ine?
Comparar
Explorar MARKO 15:34
2
MARKO 15:39
Ndipo pamene kenturiyo, woimirirapo popenyana ndi Iye, anaona kuti anapereka mzimu kotero, anati, Zoonadi, munthu uyu anali Mwana wa Mulungu.
Explorar MARKO 15:39
3
MARKO 15:38
Ndipo chinsalu chotchinga cha m'Kachisi chinang'ambika pakati, kuyambira kumwamba kufikira pansi.
Explorar MARKO 15:38
4
MARKO 15:37
Ndipo Yesu anatulutsa mau okweza, napereka mzimu wake.
Explorar MARKO 15:37
5
MARKO 15:33
Ndipo pofika ora lachisanu ndi chimodzi, panali mdima pa dziko lonse, kufikira ora lachisanu ndi chinai.
Explorar MARKO 15:33
6
MARKO 15:15
Ndipo Pilato pofuna kuwakhazika mtima anthuwo, anawamasulira Barabasi, napereka Yesu, atamkwapula, akampachike pamtanda.
Explorar MARKO 15:15
Inicio
Biblia
Planes
Vídeos