1
MACHITIDWE A ATUMWI 18:10
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
chifukwa Ine ndili pamodzi ndi iwe, ndipo palibe munthu adzautsana ndi iwe kuti akuipse; chifukwa ndili nao anthu ambiri m'mudzi muno.
Comparar
Explorar MACHITIDWE A ATUMWI 18:10
2
MACHITIDWE A ATUMWI 18:9
Ndipo Ambuye anati kwa Paulo usiku m'masomphenya, Usaope, koma nena, usakhale chete
Explorar MACHITIDWE A ATUMWI 18:9
Inicio
Biblia
Planes
Vídeos