YouVersion Logo
Search Icon

YOHANE 6:19-20

YOHANE 6:19-20 BLP-2018

Ndipo pamene adapalasa monga mastadiya makumi awiri ndi asanu kapena makumi atatu, anaona Yesu alikuyenda panyanja, ndi kuyandikira ngalawa; ndipo anachita mantha. Koma Iye ananena nao, Ndine; musaope.

Free Reading Plans and Devotionals related to YOHANE 6:19-20