YouVersion-Logo
BibelLesepläneVideos
Hol dir die App!
Sprachauswahl
Suchsymbol

Beliebte Verse in YOHANE 2

1

YOHANE 2:11

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chiyambi ichi cha zizindikiro zake Yesu anachita mu Kana wa mu Galileya naonetsera ulemerero wake; ndipo ophunzira ake anakhulupirira Iye.

Vergleichen

Studiere YOHANE 2:11

2

YOHANE 2:4

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu nanena naye, Mkazi, ndili ndi chiyani ndi inu? Nthawi yanga siinafike.

Vergleichen

Studiere YOHANE 2:4

3

YOHANE 2:7-8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende. Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao.

Vergleichen

Studiere YOHANE 2:7-8

4

YOHANE 2:19

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.

Vergleichen

Studiere YOHANE 2:19

5

YOHANE 2:15-16

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo pamene adapanga mkwapulo wazingwe, anatulutsa onse mu Kachisimo, ndi nkhosa ndi ng'ombe; nakhuthula ndalama za osinthanawo, nagubuduza magome; nati kwa iwo akugulitsa nkhunda, Chotsani izi muno; musamayesa nyumba ya Atate wanga nyumba ya malonda.

Vergleichen

Studiere YOHANE 2:15-16

Kostenlose Lesepläne und Andachten zum Thema YOHANE 2

Vorheriges Kapitel
Nächstes Kapitel
YouVersion

Die App ermutigt und fordert dich heraus, jeden Tag die Gemeinschaft mit Gott zu suchen.

Dienst

Über

Jobangebote

Ehrenamtlich helfen

Blog

Presse

Nützliche Links

Hilfe

Spenden

Bibelübersetzungen

Hörbibeln

Bibelsprachen

Vers des Tages


Ein digitaler Dienst von

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

DatenschutzrichtlinieAGB
Verfahren zur Offenlegung von Sicherheitslücken (VDP)
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Hauptbildschirm

Bibel

Lesepläne

Videos