شعار YouVersion
الكتاب المقدسخططفيديوهات
إحصل على التطبيق
مُحدد اللغة
رمز البحث

آيات مشهورة من الكتاب المقدس منGENESIS 2

1

GENESIS 2:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.

قارن

اكتشف GENESIS 2:24

2

GENESIS 2:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.

قارن

اكتشف GENESIS 2:18

3

GENESIS 2:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.

قارن

اكتشف GENESIS 2:7

4

GENESIS 2:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.

قارن

اكتشف GENESIS 2:23

5

GENESIS 2:3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Mulungu ndipo anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri, naliyeretsa limenelo: chifukwa limenelo adapuma ku ntchito yake yonse imene Mulungu anailenga ndi kupanga.

قارن

اكتشف GENESIS 2:3

6

GENESIS 2:25

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.

قارن

اكتشف GENESIS 2:25

خطط قرأة مجانية و مواضيع تعبدية ذات صلة بGENESIS 2

الإصحاح السابق
الإصحاح التالي
YouVersion

تشجع للبحث عن علاقة حميمة مع الله كل يوم.

خدمة

حول‌

مهن

التطوع

المفكّرة

صحافة

روابط مفيدة

مساعدة

تبرع

اصدارات الكتاب المقدس

الأناجيل المسموعة

لغات الكتاب المقدس

آية اليوم


خدمة رقمية ل

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

سياسة الخصوصيةالشروط
برنامج الكشف عن نقاط الضعف
فيسبوكتويترالإنستجرامموقع يوتيوببينتيريست

الصفحة الرئيسية

الكتاب المقدس

خطط

فيديوهات