1
Genesis 19:26
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Koma mkazi wa Loti anachewuka ndipo anasanduka mwala wa mchere.
對照
探尋 Genesis 19:26
2
Genesis 19:16
Koma Loti ankakayikabe. Koma Yehova anawachitira chifundo motero kuti anthu aja anagwira mkazi wake ndi ana ake aakazi aja nawatsogolera bwinobwino kuwatulutsa mu mzindawo.
探尋 Genesis 19:16
3
Genesis 19:17
Atangowatulutsa, mmodzi wa angelowo anati, “Thawani kuti mudzipulumutse, musachewuke, musayime pena paliponse mʼchigwamo! Thawirani ku mapiri kuopa kuti mungawonongeke!”
探尋 Genesis 19:17
4
Genesis 19:29
Choncho Mulungu anawononga mizinda ya ku chigwa, koma anakumbukira pemphero la Abrahamu natulutsa Loti ku sulufule ndi moto zimene zinawononga mizinda ya kumene Loti amakhalako.
探尋 Genesis 19:29
首頁
聖經
計畫
視訊