YouVersion 標誌
聖經計劃影片
現在就下載
語言選擇器
搜尋圖標

熱門經文出自 YOHANE 2

1

YOHANE 2:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chiyambi ichi cha zizindikiro zake Yesu anachita m'Kana wa m'Galileya naonetsera ulemerero wake; ndipo ophunzira ake anakhulupirira Iye.

對照

YOHANE 2:11 探索

2

YOHANE 2:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu nanena naye, Mkazi, ndili ndi chiyani ndi inu? Nthawi yanga siinafike.

對照

YOHANE 2:4 探索

3

YOHANE 2:7-8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende. Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao.

對照

YOHANE 2:7-8 探索

4

YOHANE 2:19

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.

對照

YOHANE 2:19 探索

5

YOHANE 2:15-16

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pamene adapanga mkwapulo wazingwe, anatulutsa onse m'Kachisimo, ndi nkhosa ndi ng'ombe; nakhuthula ndalama za osinthanawo, nagubuduza magome; nati kwa iwo akugulitsa nkhunda, Chotsani izi muno; musamayesa nyumba ya Atate wanga nyumba ya malonda.

對照

YOHANE 2:15-16 探索

上一章
下一章
YouVersion

每天鼓勵和挑戰你尋求與上帝的親密關係。

事工

關於

事業

義工

網誌

新聞

有用的連結

幫助

捐贈

聖經譯本

有聲聖經

聖經譯本語言

今日經文


此數字事工屬予

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

私隱政策使用條款
漏洞披露計劃
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主頁

聖經

計劃

影片