YouVersion 標誌
聖經計劃影片
現在就下載
語言選擇器
搜尋圖標

熱門經文出自 GENESIS 11

1

GENESIS 11:6-7

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anati, Taonani, anthu ali amodzi, ndipo onse ali nacho chinenedwe chao chimodzi; ndipo ichi ayamba kuchita: ndipo tsopano palibe kanthu kakuletsedwa nao kamene akafuna kuchita. Tiyeni, titsike, pomwepo tisokoneze chinenedwe chao, kuti wina asamvere chinenedwe cha mnzake.

對照

GENESIS 11:6-7 探索

2

GENESIS 11:4

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anati, Tiyeni, timange mzinda ndi nsanja, pamutu pake pafikire kumwamba; ndipo tidzipangire ife tokha dzina kuti tisabalalike padziko lonse lapansi.

對照

GENESIS 11:4 探索

3

GENESIS 11:9

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chifukwa chake anatcha dzina lake Babiloni pakuti kumeneko Yehova anasokoneza chinenedwe cha dziko lonse lapansi; kuyambira pamenepo Yehova anabalalitsa iwo padziko lonse lapansi.

對照

GENESIS 11:9 探索

4

GENESIS 11:1

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo dziko lapansi linali la chinenedwe chimodzi ndi chilankhulidwe chimodzi.

對照

GENESIS 11:1 探索

5

GENESIS 11:5

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anatsikira kudzaona mzinda ndi nsanja imene analinkumanga ana a anthu.

對照

GENESIS 11:5 探索

6

GENESIS 11:8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anabalalitsa iwo padziko lonse lapansi, ndipo analeka kumanga mzinda.

對照

GENESIS 11:8 探索

上一章
下一章
YouVersion

每天鼓勵和挑戰你尋求與上帝的親密關係。

事工

關於

事業

義工

網誌

新聞

有用的連結

幫助

捐贈

聖經譯本

有聲聖經

聖經譯本語言

今日經文


此數字事工屬予

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

私隱政策使用條款
漏洞披露計劃
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主頁

聖經

計劃

影片